LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsa. 6
  • Yesu Anali Kukonda Anthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Anali Kukonda Anthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 January tsa. 6
Yesu acilitsa munthu wakhate

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 8-9

Yesu Anali Kukonda Anthu

Macaputa 8 na 9 a Mateyu amakamba za utumiki wa Yesu m’cigawo ca Galileya. Pamene Yesu anacilitsa anthu, anaonetsa mphamvu zake, koma koposa zonse anaonetsa cikondi cake na cifundo cake kwa anthu.

  1. Mizinda ya ku Galileya imene Yesu anacilitsako anthu

    Yesu anacilitsa munthu wakhate.—Mat. 8:1-3

  2. Yesu anacilitsa kapolo wa kapitawo wa asilikali.—Mat. 8:5-13

    Anacilitsa apongozi a Petulo.—Mat. 8:14, 15

    Anatulutsa viŵanda na kucilitsa anthu osamvela bwino m’thupi.—Mat. 8:16, 17

  3. Yesu anatulutsa viŵanda voopsa n’kuvitumiza m’cigulu ca nkhumba.—Mat. 8:28-32

  4. Yesu anacilitsa munthu wakufa ziwalo.—Mat. 9:1-8

    Anacilitsa mkazi amene anagwila covala cake, ndipo anaukitsa mwana wamkazi wa Yairo.—Mat. 9:18-26

    Anacilitsa munthu wosapenya na wosakamba.—Mat. 9:27-34

  5. Yesu anali kupita m’mizinda na m’midzi, kucilitsa matenda a mtundu uliwonse na zofooka zilizonse.—Mat. 9:35, 36

Ningacite ciani kuti nizionetsa kwambili cikondi na cifundo kwa anthu amene nimakhala nawo?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani