LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsa. 2
  • Pasika na Cikumbutso—Kulingana na Kusiyana Kwake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Pasika na Cikumbutso—Kulingana na Kusiyana Kwake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • ‘Ici Cidzakhala Cikumbutso Kwa Inu’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2024
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 April tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | MATEYU 26

Pasika na Cikumbutso—Kulingana na Kusiyana Kwake

26:18

Nkhosa ya pa Pasika, mkate wopanda cofufumitsa, ndiyo zoŵaŵa zamasamba, na vinyo

Lembani maina a zinthu pa manamba ali pansipa.

1

2

3

4

Pa zinthu izi, ni ziti zimene zimasewenzetsewa pa Mgonelo wa Ambuye?

KODI MUDZIŴA?

Ngakhale kuti Pasika siinali kucitila cithunzi Cikumbutso, zinthu zina za pa Pasika zili na tanthauzo kwa ise. Mwacitsanzo, mtumwi Paulo anachula Yesu kuti “nsembe yathu ya Pasika.” (1 Akor. 5:7) Monga mmene magazi a nkhosa amene anawazidwa pa zitseko anapulumutsila miyoyo, nawonso magazi a Yesu amapulumutsa miyoyo. (Eks. 12:12, 13) Cina, panalibe fupa la nkhosa ya pa Pasika imene inathyoledwa. Mofananamo, palibe ngakhale fupa limodzi la Yesu limene linathyoledwa, olo kuti panthawiyo unali mwambo kuthyola mafupa a munthu amene wapacikiwa.—Eks. 12:46; Yoh. 19:31-33, 36.

Yesu akhazikitsa mwambo wa Mgonelo wa Ambuye
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani