LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsa. 7
  • Mwana Woloŵelela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mwana Woloŵelela
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuseŵenzetsa Mavidiyo Pophunzitsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Kodi ‘Mumamvetsa Tanthauzo la Malemba’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 July tsa. 7
David wabwelela, ndipo akukumbatilana na atate ake

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Mwana Woloŵelela

TAMBANI VIDIYO YAKUTI MWANA WOLOWELELA, NDIYENO YANKHANI MAFUNSO OTSATILAWA:

  • N’ciani cinaonetsa kuti David wayamba kupatuka pa njila ya coonadi? Nanga a m’banja mwake na akulu anayesa kumuthandiza bwanji?

  • Kodi M’bale na Mlongo Barker, monga makolo, anali citsanzo cabwino motani?

  • Kodi vidiyoyi yatiphunizitsa ciani ponena za . . .

    • David na Alani aseŵenzela pamodzi

      kudzipeleka pa nchito zakuthupi?

    • David na Alani ali ku baa pamodzi na Vivian komanso Tala

      mayanjano oipa?

    • David amvetsela pamene atate ake akum’patsa uphungu wocokela m’Baibo

      kumvela uphungu?

    • A John Barker akamba na James, mwana wawo wamkulu.

      kulapa na kukhululuka?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani