LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsa. 2
  • Yesu Amasamalila Nkhosa Zake

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yesu Amasamalila Nkhosa Zake
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • “Nkhosa Zosocela Ndidzazifunafuna”
    Bwelelani kwa Yehova
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 October tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 9-10

Yesu Amasamalila Nkhosa Zake

10:1-5, 11, 14, 16

M’busa amakhala pa ubwenzi wabwino na nkhosa zake cifukwa ca kudziŵana na kukhulupililana. Yesu, amene ni M’busa Wabwino, amadziŵa nkhosa iliyonse payokha—zimene imasoŵeka, zofooka zake, komanso mphamvu zake. Nkhosa zimamudziŵa m’busa wawo, ndipo zimakhulupilila utsogoleli wake.

Ni motani mmene Yesu, M’busa Wabwino, . . .

  • amasonkhanitsila nkhosa zake?

  • amatsogolela nkhosa zake?

  • amatetezela nkhosa zake?

  • amadyetsela nkhosa zake?

M’busa akulonda pa khomo la khola la nkhosa

ZOFUNIKA KUSINKHA-SINKHA: Ningaonetse bwanji kuti nimayamikila kwambili cisamalilo ca Yesu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani