LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 December tsa. 7
  • “Mukhale Chelu ndi Kuyang’anila Gulu Lonse la Nkhosa”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Mukhale Chelu ndi Kuyang’anila Gulu Lonse la Nkhosa”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Nkhani Zofanana
  • Abusa, Tsanzilani Abusa Aakulu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • “Mfumu Idzalamulila Mwacilungamo”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
  • Muzimvela Abusa A Yehova
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 December tsa. 7
Akulu akukamba na anthu pa Nyumba ya Ufumu

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 19-20

“Mukhale Chelu ndi Kuyang’anila Gulu Lonse la Nkhosa”

20:28, 31, 35

Mkulu akukamba na dokota m’cipatala pamene m’bale ali gone pa bed

Akulu amadyetsa nkhosa, kuziteteza na kuzisamalila. Amakumbukila kuti nkhosa iliyonse inagulidwa na magazi a mtengo wapatali a Khristu. Abale na alongo amakonda na kuyamikila akulu amene amadzipeleka mofunitsitsa kuti asamalile nkhosa, monga mmene Paulo anacitila.

Dzifunseni kuti, ‘Nimaonetsa bwanji kuti nimayamikila khama la akulu a mumpingo mwathu?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani