LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsa. 6
  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Yobu Anali ndi Cikhulupililo Cakuti Akufa Adzauka
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 February tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 9-11

Fanizo la Mtengo wa Maolivi

11:16-26

Kodi mbali zosiyana-siyana za mtengo wophiphilitsa wa maolivi ziimila ciani?

Mtengo wophiphilitsa wa maoli wochulidwa pa Aroma 11
  • Mtengo: kukwanilitsidwa kwa colinga ca Mulungu cokhudza cipangano ca Abulahamu

  • Thunthu: Yesu, mbali yaikulu ya mbewu ya Abulahamu

  • Nthambi: a 144,000 amene apanga mbali yaciŵili ya mbewu ya Abulahamu

  • Nthambi ‘zodulidwa’: Ayuda amene anakana Yesu

  • Nthambi ‘zolumikizidwa’: Akhristu odzozedwa na mzimu ocokela m’mitundu yonse

Monga mwa ulosi, mbewu ya Abulahamu, kutanthauza Yesu na a 144,000, adzabweletsa madalitso kwa “anthu a mitundu.”—Aroma 11:12; Gen. 22:18

Niphunzilapo ciani pa mmene Yehova anakwanilitsila colinga cake cokhudza mbewu ya Abulahamu?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani