LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsa. 2
  • Vulani Umunthu Wakale, Muvale Watsopano

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Vulani Umunthu Wakale, Muvale Watsopano
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • N’zotheka ‘Kuvula Umunthu Wakale’
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Pitilizani Kuvala “Umunthu Watsopano” Pambuyo pa Ubatizo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Mmene Timavalila Umunthu Watsopano ndi Kusauvulanso
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Mmene Timavulila Umunthu Wakale ndi Kusauvalanso
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 July tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AKOLOSE 1-4

Vulani Umunthu Wakale, Muvale Watsopano

3:5-14

Mlongo akusinkha-sinkha pambuyo poŵelenga buku yakuti Yandikirani kwa Yehova, ndiponso Baibo

Kodi munasintha kwambili umunthu wanu mutabwela m’coonadi? Mosakayikila Yehova anakondwela cifukwa ca kuyesetsa kwanu kuti musinthe. (Ezek. 33:11) Komabe, kulimbikila n’kofunika kuti munthu asabwelelenso ku makhalidwe akale, na kuti apitilize kuvala umunthu watsopano. Yankhani mafunso otsatilawa kuti muone mbali zimene mungafunike kuwongolela:

  • Kodi pali amene n’nasungila cakukhosi cifukwa conilakwila?

  • Kodi nimakhalabe woleza mtima ngakhale pamene nili wofulumila kapena wolema?

  • Kodi malingalilo osayenela akabwela m’maganizo mwanga nimayacotsa mwamsanga?

  • Kodi nimaipidwa nawo anthu a mtundu wina kapena ocoka ku maiko ena?

  • Kodi posacedwa n’nazazilapo munthu aliyense kapena kumukwiyila?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani