LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsa. 6
  • Kudzipeleka kwa Mulungu Kapena ku Cuma

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kudzipeleka kwa Mulungu Kapena ku Cuma
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 July tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 TIMOTEYO 4-6

Kudzipeleka kwa Mulungu Kapena ku Cuma

6:6-10

Kodi malemba otsatilawa, aonetsa bwanji kuti tingakhale acimwemwe kwambili ngati tadzipeleka kwa Mulungu m’malo mofuna-funa cuma?

  • Mlongo aika pa bodi mapikica a mautumiki osiyana-siyana amene anacitako mu utumiki wa nthawi zonse

    Anthu amene amayamba utumiki wa nthawi zonse amapeza madalitso

    Mlal. 5:10

  • Mlal. 5:12

  • Mat. 5:3

  • Mac. 20:35

N’cifukwa ciani n’zosatheka kucita zonse ziŵili panthawi imodzi, kudzipeleka kwa Mulungu komanso ku Cuma? (Mat. 6:24)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani