LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsa. 6
  • Zimene Zimabweletsa Macimo na Imfa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Zimabweletsa Macimo na Imfa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • “Mukhale Oyela”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo pa Dziko Lapansi
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Musalole Zilakolako Zoipa Kukulamulilani
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • “Sandulikani mwa Kusintha Maganizo Anu”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 September tsa. 6
M’bale akuganizila mayeselo osiyana-siyana: ndalama, motoka yocitila mpikisano, fodya, mkazi amene amamukopa

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YAKOBO 1-2

Zimene Zimabweletsa Macimo na Imfa

1:14, 15

Ngati mwayamba kuganizila zinthu zolakwika, citani izi:

  • Yambani kuganizila zinthu zina zabwino.—Afil. 4:8

  • Ganizilani mavuto amene mungakumane nawo ngati mwagonja ku ciyeselo.—Deut. 32:29

  • Pemphelani.—Mat. 26:41

izila zinthu zolakwika, ni zinthu zolimbikitsa ziti zimene mungaganizile m’malomwake?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani