LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 December tsa. 4
  • Musamaope Zilombo Zoopsa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musamaope Zilombo Zoopsa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Buku la Chivumbulutso—Cimene Cidzacitikila Adani a Mulungu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 December tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | CHIVUMBULUTSO 13-16

Musamaope Zilombo Zoopsa

13:1, 2, 11, 15-17

Kumvetsetsa zimene zilombo zochulidwa mu Chivumbulutso caputa 13 zimaimila, kumatithandiza kupewa kuziyopa kapena kuzikhumbila na kuzicilikiza monga mmene anthu ena amacitila.

GWILIZANITSANI CILOMBO CILICONSE NA ZIMENE CIIMILA

ZILOMBO

Cilombo ca mitu 7

Cinjoka.—Chiv. 13:, ftn.

Cilombo ca mitu 7

Cilombo ca nyanga 10 na mitu 7.—Chiv. 13:1, 2

Cilombo ca nyanga ziŵili

Cilombo ca nyanga ziŵili ngati mwana wa nkhosa.—Chiv. 13:11

Cifanizilo ca cilombo

Cifanizilo ca cilombo.—Chiv. 13:15

MAULAMULILO

  • Ulamulilo wamphamvu padziko lonse wa Britain na America

  • Bungwe la League of Nations komanso United Nations

  • Satana Mdyelekezi

  • Maboma onse otsutsana na Mulungu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani