LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsa. 2
  • Cipangano Cimene Cimakukhudzani

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Cipangano Cimene Cimakukhudzani
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Mudzakhala “Ufumu wa Ansembe”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
  • Khalani ndi Cikhulupililo Cosagwedela mu Ufumu
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2014
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 February tsa. 2
Abulahamu akuyang’ana kumwamba kodzala na nyenyezi.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 12-14

Cipangano Cimene Cimakukhudzani

12:1-3; 13:14-17

  • Yehova anacita cipangano na Abulahamu, cimene cinakhala maziko a Ufumu wa kumwamba

  • Cipangano cimeneco ciyenela kuti cinayamba kugwila nchito mu 1943 B.C.E. pamene Abulahamu anawoloka Mtsinje wa Firate ali pa ulendo wopita ku Kanani

  • Cipanganoco cidzagwilabe nchito mpaka pamene Ufumu wa Mesiya udzawononga adani a Mulungu na kubweletsa madalitso ku mabanja onse pa dziko lapansi

Yehova anadalitsa Abulahamu cifukwa ca cikhulupililo cacikulu. Ngati tikhulupilila malonjezo a Yehova, kodi tidzalandila madalitso otani cifukwa ca cipangano ca Abulahamu?

Abulahamu komanso a m’banja lake apitilila mudzi winawake m’dziko la Kanani paulendo wawo.
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani