LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsa. 4
  • Tamandani Yehova mwa Kuimba Nyimbo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tamandani Yehova mwa Kuimba Nyimbo
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Muziimba Mosangalala!
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 August tsa. 4

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKSODO 15-16

Tamandani Yehova mwa Kuimba Nyimbo

15:1, 2, 11, 18, 20, 21

Nyimbo zimakhudza kwambili maganizo athu na mmene timamvelela mumtima. Ndipo kuimba nyimbo ni mbali yofunika kwambili pa kulambila kwathu Yehova.

  • Mose na Aisiraeli akuimbila Yehova nyimbo yacipambano.

    Mose na Aisiraeli anaimbila zitamando Yehova cifukwa cakuti anawapulumutsa mozizwitsa pa Nyanja Yofiila

  • Alevi akuliza malipenga ndipo akuimba polambila Yehova.

    Mfumu Davide anaika amuna 4,000 kuti azicita utumiki woimba nyimbo pa kacisi

  • Yesu na atumwi ake okhulupilika akuimbila Yehova zitamando.

    Usiku wakuti aphedwa maŵa, Yesu pamodzi na atumwi ake okhulupilika anaimba nyimbo zotamanda Yehova

Kodi ni mipata iti imene ningamaiseŵenzetse poimba nyimbo zotamanda Yehova?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani