LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsa. 6
  • Kupeleka kwa Yehova Copeleka

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kupeleka kwa Yehova Copeleka
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
  • Nkhani Zofanana
  • Nchito Yomanga Imene Imalemekeza Yehova
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
  • Awa Ndi Malo Athu Olambilila
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Timamangilanji Nyumba za Ufumu, Nanga Timamanga Bwanji?
    Ndani Amene Akucita Cifunilo Ca Yehova Masiku Ano?
  • Mmene Timapezela Ndalama Zoyendetsela Nchito za Ufumu
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulila
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 September tsa. 6
M’bale akuika copeleka m’bokosi ya zopeleka.

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | EKSODO 29–30

Kupatsa Yehova Copeleka

30:11-16

Pamene cihema cinapangidwa, munthu aliyense anali na mwayi wopeleka ndalama kuti acilikize kulambila Yehova, mosasamala kanthu kuti anali wolemela kapena wosauka. Kodi tingacite bwanji copeleka kwa Yehova masiku ano? Njila imodzi ni mwa kupeleka ndalama zocilikiza Nyumba za Ufumu, Mabwalo a Misonkhano, ma Ofesi Omasulila Mabuku, komanso malo a Beteli, kuphatikizapo zimango zina zimene zimagwilitsidwa nchito polambila Yehova.

Tiphunzilapo ciani pa malemba otsatilawa pa nkhani yocita copeleka cocilikiza kulambila koona?

  • 1 Mbiri 29:5

  • Maliko 12:43, 44

  • 1 Akor. 16:2

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani