LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsa. 14
  • Kodi Mumaugwila Mtima?

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kodi Mumaugwila Mtima?
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Citsanzo Cimene Tingatengele pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Mukhuthulileni za Mumtima Mwanu Yehova M’pemphelo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Abigayeli Ndi Davide
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Kodi Mukayika-kayika Mpaka Liti?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 March tsa. 14
Zithunzi: 1. Davide akuimitsa asilikali ake atakumana na Abigayeli na atumiki ake amene anyamula zakudya. 2. Abigayeli wagwada modzicepetsa pamaso pa Davide, ndipo akukamba mom’condelela.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mumaugwila Mtima?

Pempho la Davide linali loyenela, koma Nabala anam’nyoza Davide pamodzi na asilikali ake (1 Sam. 25:7-11; ia 78 ¶10-12)

Davide posaugwila mtima anafuna kupha amuna a m’nyumba ya Nabala (1 Sam. 25:13, 21, 22)

Abigayeli anathandiza Davide kupewa kupalamula mlandu wa magazi (1 Sam. 25:25, 26, 32, 33; ia 80 ¶18)

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi nimalephela kudziletsa nikakwiya, nikamagula zinthu, kapena nikalefulidwa? Kapena nimaima na kuganizila zotulukapo zake n’sanacitepo kanthu?’—Miy. 15:28; 22:3.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani