LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsa. 3
  • Dzilimbitseni mwa Yehova Mulungu Wanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Dzilimbitseni mwa Yehova Mulungu Wanu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Yembekezelani Yehova Moleza Mtima
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mukhuthulileni za Mumtima Mwanu Yehova M’pemphelo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Kumvela Kumaposa Nsembe
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Khalanibe Odzicepetsa Zinthu Zikakuyendelani Bwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 May tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Dzilimbitseni mwa Yehova Mulungu Wanu

Aamaleki anatentha mzinda wa Zikilaga n’kutenga anthu a mumzindawo kuti akakhale akapolo awo (1 Sam. 30:1, 2)

Davide na amuna amene anali naye anavutika kwambili maganizo (1 Sam 30:3-5; w06 8/1 28 ¶12)

Davide anapeza mphamvu mwa Yehova (1 Sam. 30:6; w12 4/15 30 ¶14)

M’bale wopsinjika maganizo waika felemu ya cithunzi pacifuwa pake.

ZOYENELA KUZIGANIZILA: Nikapanikizika maganizo, kodi nimapeza mphamvu kwa ndani?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani