LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsa. 7
  • Musakhale na Nkhawa Mukakumana na Mavuto Azacuma

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musakhale na Nkhawa Mukakumana na Mavuto Azacuma
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Mulungu Wathu Amationa Kuti Ndife Ofunika
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
  • Pitilizani Kuyembekezela Mopilila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Kodi Cikhulupililo Canu Cidzakhala Colimba Motani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Tengelani Citsanzo kwa Aneneli—Habakuku
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 September tsa. 7
Zithunzi zoonetsa zocitika za mu vidiyo yakuti “Mangani Nyumba Imene Idzakhalitsa—‘Khutilani Ndi Zimene Muli Nazo pa Nthawiyo.’” Zithunzi: 1. M’bale Ángel akuŵelenga Baibo. 2. M’bale Lester na mkazi wake akuŵelenga Baibo.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Musakhale na Nkhawa Mukakumana na Mavuto Azacuma

Umoyo masiku otsiliza ano ni wodzala na mavuto. Ndipo n’zodziŵikilatu kuti pamene mapeto a dzikoli akuyandikila, mavuto aziculukila-culukila. Tingasoŵe zinthu zina zofunika pa umoyo. (Hab. 3:16-18) N’ciyani cingatithandize kuti tisamakhale na nkhawa tikakumana na mavuto azacuma? Sitiyenela kuleka kudalila Mulungu wathu, Yehova. Iye analonjeza kuti adzasamalila atumiki ake, ndipo olo zinthu zivute bwanji, adzatithandiza kupeza zosowa zathu.—Sal. 37:18, 19; Aheb. 13:5, 6.

Zimene mungacite:

  • Pemphani Yehova kuti akutsogoleleni, akupatseni nzelu, na kukuthandizani.—Sal. 62:8

  • Khalani okonzeka kugwila nchito imene simunaigwilepo.—g 1/10 8-9, mabokosi

  • Musaleke cizoloŵezi canu cocita zinthu zauzimu, monga kuŵelenga Mawu a Mulungu tsiku lililonse, kupezeka ku misonkhano ya mpingo, na kulalikila

ONELELANI VIDIYO YAKUTI MANGANI NYUMBA IMENE IDZAKHALITSA—‘KHUTILANI NDI ZIMENE MULI NAZO PA NTHAWIYO,’ KENAKO YANKHANI MAFUNSO AWA:

  • Kodi mabanja ena akukumana na mavuto otani?

  • N’ciyani cofunika kwambili pa umoyo?

  • Kodi amene akukumana na mavuto azacuma tingawathandize bwanji?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani