LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mfundo ya Kumapeto

^ [1] (palagilafu 14) Pali zolinganako zambili pakati pa ukapolo wa Ayuda wa zaka 70 ku Babulo, na zimene zinacitika kwa Akhiristu mpatuko utayamba. Komabe, sizikuoneka kuti ukapolo wa Ayuda kweni-kweni unacitila cithunzi zimene zinali kudzacitika kwa Akhiristu. Mwacitsanzo, utali wa zaka za ukopolo unali wosiyana. Conco, sitiyenela kuyesa kugwilizanitsa mbali zonse-zonse za ukapolo wa Ayuda ndi zimene zinacitika kwa Akhiristu odzozedwa m’zaka zokafikitsa ku 1919.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani