Mawu Amunsi
a Anthu ena ocepa angakhale na cisoni cacikulu kwambili ndipo cingatenge nthawi yaitali. Cisoni cimeneci cimachedwa cisoni “cocolowana” kapena “cokhalitsa.” Anthu aconco angafunikile kukaonana na madokota opeleka cithandizo kwa anthu ovutika maganizo.