LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Koran imakamba za kubadwa kwa Yesu kozizwitsa pa Surah 19 (Mariya). Imati: “Tinatumiza mzimu Wathu kwa [Mariya] wooneka ngati munthu wamkulu. Ndipo pamene iye anauona anati: ‘Wacifundoyo andichinjilize kwa inu! Ngati mumaopa Ambuye, mundisiye ndi kupitiliza ulendo wanu.’ Koma mzimu unayankha kuti: ‘Ndine mthenga wa Ambuye wako, ndipo ndabwela kukupatsa mwana woyela.’ Iye anayankha kuti: ‘Ndingabale bwanji mwana ine namwali wosadziŵa mwamuna?’ Poyankha mzimu unati: ‘Ndi cifunilo ca Ambuye. Izi si zovuta kwa Iye. Ambuye ati: “Mwana ameneyo adzakhala cizindikilo kwa anthu onse ndi dalitso locokela kwa Ife. Uthenga Wathu ndi umeneo.”’”

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani