LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a M’malemba Aciheberi mulibe liu lenileni lotanthauza “cikumbumtima.” Komabe mogwilizana ndi citsanzo ici, pali umboni woonekelatu wakuti anthu anali kumvela cikumbumtima cao. Liu lakuti “mtima” nthawi zambili limatanthauza munthu wamkati. Koma pa lembali, liu limeneli limakamba za cikumbumtima, cimene ndi mbali imodzi cabe ya munthu wamkati. Liu la Cigiriki lotembenuzidwa kuti “cikumbumtima” limaonekela nthawi 30 m’Malemba Acigiriki Acikristu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani