Mawu Amunsi
c Anthu olemba mabuku ofotokoza Baibulo amati mau aciheberi pa lembali, “amaonetsa kuti mau amenewa sakamba za kuvulala kwa mai yekha.” Ndipo Baibulo silinena kuti Yehova anali kupeleka ciweluzo modalila miyezi ya mwana amene ali m’mimba.