LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c Cinthu cina cimene cinapangitsa kuti Ophunzila Baibulo ena aone macenjezowo mopepuka cinali cakuti macenjezowo anali kupelekedwa makamaka kwa a 144,000, amene ndi kagulu ka nkhosa ka Kristu. M’Nkhani 5 tidzaona kuti caka ca 1935 cisanafike, Ophunzila Baibulo anali kukhulupilila kuti “khamu lalikulu,” monga mmene lafotokozedwela pa Chivumbulutso 7:9, 10, lidzaphatikizapo mamembala ambilimbili a machalichi acikristu. Anali kukhulupililanso kuti anthu amenewa adzakhala m’gulu laciŵili la anthu amene adzapita kumwamba cifukwa cocilikiza Kristu m’nthawi yamapeto.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani