Mawu Amunsi
c Pamene cigamuloco cinasitha, boma la Bulgaria linafunika kupezela nchito zina anthu amene sanali kufuna kugwila nchito za usilikali cifukwa ca cikumbumtima cao. Linafunika kuwapezela nchito zimene sizinali kuyang’anilidwa ndi asilikali.