LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kodi timadziŵa bwanji kuti Atate anaphunzitsa Mwana wake mmene angaphunzitsile ena? Ganizilani izi: Yesu anali kukonda kugwilitsila nchito mafanizo polalikila, ndipo zimenezi zinakwanilitsa ulosi umene unalembedwa zaka zambilimbili iye asanabadwe. (Sal. 78:2; Mat. 13:34, 35) Mwacionekele, Mlembi wamkulu wa ulosiwo, Yehova, anadziŵilatu kuti Mwana wake adzagwilitsila nchito mafanizo pophunzitsa.—2 Tim. 3:16, 17.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani