Mawu Amunsi
a “Nkhosa zina” za Yesu zidzakhala ana a Mulungu pamapeto pa zaka 1,000. Komabe, cifukwa coti iwowa anadzipatulila kwa Mulungu, angathe kuchula Mulungu kuti “Atate” ndipo amaonedwa kuti ali m’banja la olambila Yehova.—Yoh. 10:16; Yes. 64:8; Mat. 6:9; Chiv. 20:5.