Mawu Amunsi
b Mfundo imeneyi ni yosiyana na zimene Baibo imaphunzitsa cifukwa Baibo imaphunzitsa kuti zonse zimene Mulungu analenga zinali zabwino. Imafotokozanso kuti pali wina amene anayambitsa zoipa. (Deuteronomo 32:4, 5) Yehova atamaliza kulenga zinthu padziko lapansi ananena kuti zonse zimene analengazo “zinali zabwino kwambili.”—Genesis 1:31.