LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Ndime 8: Mbali imodzi ya zocitika zochulidwa m’mavesi amenewa ndi ‘kusonkhanitsidwa kwa osankhidwa.’ (Mat. 24:31) Conco, zikuoneka kuti odzozedwa onse amene adzakhalabe padziko lapansi pambuyo pakuti mbali yoyamba ya cisautso cacikulu yatha, adzatengedwa kupita kumwamba nkhondo ya Aramagedo isanayambe. Zimenezi zasintha mfundo zimene zinafotokozedwa mu Nsanja ya Olonda ya August 15, 1990, patsamba 30, pa mutu wakuti “Mafunso Ocokela kwa Oŵelenga.”

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani