Mawu Amunsi
b Ndime 3: Popeza atumwi a Yesu anali atafa ndipo odzozedwa amene anali padziko lapansi sanawayelekezele ndi akapolo koma anawayelekezela ndi tiligu, akapolo amenewa amaimila angelo. Cakumapeto kwa fanizo limeneli, Yesu ananena kuti, okolola namsongole ndi angelo.—Mat. 13:39.