LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

e Ndime 14: Kumeneku ndi kusintha kwa kamvedwe kathu ka lemba la Mateyu 13:42. M’mbuyomu, zofalitsa zathu zinali kufotokoza kuti Akristu onama akhala akulila ndi kukukuta mano kwa zaka zambili cifukwa cakuti, “ana a ufumu” akhala akuwavumbula kuti io ndi “ana a woipayo.” (Mat. 13:38) Komabe, zimene tiyenela kudziŵa ndi zakuti, kukukuta mano kumeneku ndi kogwilizana ndi cionongeko.—Sal. 112:10.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani