LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c Ndime 8: Mfundo yakuti okhulupilila atsopano “anapitiliza kulabadila zimene atumwiwo anali kuphunzitsa,” imatanthauza kuti atumwi anali kuphunzitsa nthawi zonse. Zinthu zina zimene atumwi anali kuphunzitsa zinalembedwa m’mabuku ouzilidwa amene pa nthawi ino ndi mbali ya Malemba Acigiriki Acikristu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani