Mawu Amunsi
c Ndime 8: Mfundo yakuti okhulupilila atsopano “anapitiliza kulabadila zimene atumwiwo anali kuphunzitsa,” imatanthauza kuti atumwi anali kuphunzitsa nthawi zonse. Zinthu zina zimene atumwi anali kuphunzitsa zinalembedwa m’mabuku ouzilidwa amene pa nthawi ino ndi mbali ya Malemba Acigiriki Acikristu.