Mawu Amunsi
e Ndime13: Mau a mtumwi Paulo pa Machitidwe 20:29, 30, amaonetsa kuti mpingo udzaukilidwa kucokela ku mbali ziŵili. Mbali yoyamba, Akristu onama (“namsongole”) ‘adzafika pakati’ pa Akristu oona. Mbali yaciŵili, “pakati” pa Akristu oona padzakhala ampatuko amene adzalankhula “zinthu zopotoka.”