Mawu Amunsi
a Ena amanena kuti Mulungu anacititsa nyamazo kuti zikhale mu mkhalidwe wosakhoza kucita kanthu kalikonse, conco sizinali kumva njala kwambili. Kaya anacita zimenezo kapena ai, Mulungu anasungabe lonjezo lake, ndi kutsimikiza kuti anthu onse amene anali m’cingalawa atetezedwa ndi kupulumutsidwa kuphatikizapo nyama.