Mawu Amunsi
b Kuonjezela pamenepa, Munda wa Edeni kunalibenso mwina cifukwa cakuti unafafanizidwa ndi madzi a cigumula. Ngati zinali conco, akelubi amene anali kulondela pa cipata ca mundawo anamasuka panthawiyo ndipo anabwelela kumwamba cifukwa cakuti nchito yao ya zaka 1600 inali itatha.—Genesis 3:22-24.