LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Kuonjezela pamenepa, Munda wa Edeni kunalibenso mwina cifukwa cakuti unafafanizidwa ndi madzi a cigumula. Ngati zinali conco, akelubi amene anali kulondela pa cipata ca mundawo anamasuka panthawiyo ndipo anabwelela kumwamba cifukwa cakuti nchito yao ya zaka 1600 inali itatha.—Genesis 3:22-24.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani