Mawu Amunsi
b Cikondwelelo ca Mikate Yopanda Cofufumitsa cinali kuyamba dzuŵa likaloŵa pa Nisani 15. Nthawi zonse, tsiku loyamba la cikondwelelo cimeneci linali kuchedwa sabata. M’caka ca 33 C.E., tsiku la Nisani 15 linalinso tsiku la Sabata la mlungu ndi mlungu (pa Ciŵelu). Tsikuli linachedwa Sabata “lalikulu” cifukwa cakuti masabata aŵili anacitika pa tsiku limodzi.—Ŵelengani Yohane. 19:31, 42.