Mawu Amunsi
a Aisiraeli anali kulambila Baala cifukwa anali kuganiza kuti ndi amene anali kubweletsa mvula ndi kupangitsa nthaka kukhala ya conde. Conco, Yehova anacititsa cilala m’dzikolo kwa zaka zitatu ndi hafu n’colinga cakuti aonetse kuti Baala ndi wopanda mphamvu. (1 Mafumu caputala 18) Onani nkhani za mutu wakuti “Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo” zopezeka m’magazini a Nsanja ya Olonda a January 1 ndi April 1, 2008.