Mawu Amunsi
a Ngati tifuna kuti Mulungu azimvela mapemphelo athu, tiyenela kucita zimene amafuna ndi mtima wonse. Tikacita zimenezo tidzaona kufunika kwa pemphelo, monga mmene nkhani ino ifotokozela. Kuti mudziŵe zambili, onani nkhani 17 m’buku lakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni, yofalitsidwa ndi Mboni za Yehova. Mungaonenso Webusaiti yathu ya www.jw.org.