Mawu Amunsi
c Nthawi zonse ana a Yakobo akasiya mabanja ao ndi kupita ku Iguputo ayenela kuti anali kukhala kumeneko milungu yosaposa itatu. Koma pamene Yakobo ndi ana ake aamuna anasamukila ku Iguputo, io anatenga akazi ndi ana ao.—Gen. 46:6, 7.
c Nthawi zonse ana a Yakobo akasiya mabanja ao ndi kupita ku Iguputo ayenela kuti anali kukhala kumeneko milungu yosaposa itatu. Koma pamene Yakobo ndi ana ake aamuna anasamukila ku Iguputo, io anatenga akazi ndi ana ao.—Gen. 46:6, 7.