LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

e Malipoti a m’maiko ambili aonetsa kuti kusakhala pamodzi monga banja kwabweletsa mavuto aakulu. Ena mwa mavutowa ndi kucita cigololo, kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha, kapena kugonana ndi wacibale. Ndipo ana sangazicita bwino ku sukulu, angakhale aukali, ankhawa, ovutika maganizo kapena angakhale ndi maganizo ofuna kudzipha.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani