Mawu Amunsi
e Malipoti a m’maiko ambili aonetsa kuti kusakhala pamodzi monga banja kwabweletsa mavuto aakulu. Ena mwa mavutowa ndi kucita cigololo, kugonana kwa amuna kapena akazi okhaokha, kapena kugonana ndi wacibale. Ndipo ana sangazicita bwino ku sukulu, angakhale aukali, ankhawa, ovutika maganizo kapena angakhale ndi maganizo ofuna kudzipha.