Mawu Amunsi
a Charles Darwin, m’buku lake lakuti The Descent of Man, anachula ziwalo zathupi zingapo kuti “n’zosafunika kwenikweni.” Munthu wina wophunzitsa za cisanduliko anakamba kuti ziwalo zambili m’thupi la munthu n’zosafunika, monga kapamba.
a Charles Darwin, m’buku lake lakuti The Descent of Man, anachula ziwalo zathupi zingapo kuti “n’zosafunika kwenikweni.” Munthu wina wophunzitsa za cisanduliko anakamba kuti ziwalo zambili m’thupi la munthu n’zosafunika, monga kapamba.