LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Buku lakuti Insight on the Scriptures, voliyamu 2 tsamba 247, limakamba kuti asayansi poyesa kufotokoza zimene zimacititsa kuti tizikalamba ndi kufa, amaiŵala mfundo imodzi yofunika. Iwo amalephela kuzindikila kuti Mlengi ndiye anaweluza anthu oyamba kuti azifa. Ndiye cifukwa cake samvetsetsa cimene cimacititsa kuti tizikalamba ndi kufa.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani