LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a M’fanizo limeneli, pali nyengo ya nthawi kucokela pamene mau akuti “Mkwati uja wafika!” akumveka (vesi 6) ndi kubwela kapena kufika kwa mkwati (vesi 10). M’masiku otsiliza ano, odzozedwa apitilizabe kukhala maso. Iwo aona cizindikilo ca kukhalapo kwa Yesu, ndipo akudziŵa kuti iye akulamulila monga Mfumu ya Ufumu wa Mulungu. Ngakhale zili conco, io afunika kukhalabe maso mpaka iye atabwela kapena kufika.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani