Mawu Amunsi
c Matupi a nyama a odzozedwa amene adzakhala ndi moyo panthawiyo sadzatengedwa kupita kumwamba. (1 Akor. 15:48, 49) Yesu sanapite kumwamba ndi thupi la nyama, naonso odzozedwa sadzapita kumwamba ndi matupi ao a nyama.
c Matupi a nyama a odzozedwa amene adzakhala ndi moyo panthawiyo sadzatengedwa kupita kumwamba. (1 Akor. 15:48, 49) Yesu sanapite kumwamba ndi thupi la nyama, naonso odzozedwa sadzapita kumwamba ndi matupi ao a nyama.