Mawu Amunsi
a Anthu ambili aona kuti Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika ni lolongosoka, lodalilika, ndi losavuta kumva. Baibo imeneyi ni yomasulidwa na Mboni za Yehova, ndipo ipezeka m’zitundu zoposa 130. Mungacite daunilodi Baibo imeneyi pa webusaiti ya jw.org kapena mungacite daunilodi JW Library. Ndipo ngati mufuna, mungapemphe a Mboni za Yehova kuti akubweletseleni Baibo kunyumba kwanu.