LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Akatswili ena a Baibo amakamba kuti Yuda anagwila mau buku lina-lake lochedwa Buku la Inoki. Koma buku limeneli ndi lokayikitsa ndipo amene analemba sadziŵika, ngakhale kuti ena amanama kuti linalembedwa ndi Inoki. M’buku limeneli muli ulosi wazoona wa Inoki, koma cioneka kuti mau a ulosi amenewa anatengedwa ku zolemba zakale zimene masiku ano kulibe, kapena ku nkhani zimene anthu anali kukamba. Mwina Yuda nayenso anatenga ulosi wa Inoki kucokela ku magwelo akale amenewa. N’kuthekanso kuti Yuda anaphunzila za Inoki kucokela kwa Yesu. Yesu anali kuona zocita za Inoki cifukwa cakuti pamene Inoki anali na moyo pa dziko lapansi, Yesuyo anali kumwamba.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani