LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Sara anali mlongosi wa Abulahamu. Atate awo anali Tera, koma amayi awo anali osiyana. (Genesis 20:12) Ngakhale kuti ukwati waconco si woyenela masiku ano, n’kofunika kuganizila mmene zinthu zinalili kalelo. Anthu anali pafupi na ungwilo umene Adamu na Hava anataya. Conco, kwa iwo kukwatilana ndi wacibululu sikunabweletse vuto lililonse kwa ana amene anali kubeleka. Koma patapita zaka 400, anthu anali atatalikilana kwambili na ungwilo. Panthawi imeneyo, Cilamulo ca Mose cinaletsa vikwati va pacibululu.—Levitiko 18:6.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani