Mawu Amunsi
a Mwacionekele, Yehova anafuna kuti pakhale atumwi 12 kuti akakhale “miyala yomangila maziko yokwana 12” a Yerusalemu Watsopano. (Chiv. 21:14) Conco, panalibe cifukwa cosankhila munthu wina kuti aloŵe m’malo mtumwi wokhulupilika aliyense amene anatsiliza utumiki wake wa padziko lapansi.