LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

c Abale othaŵa kwawo akangofika, akulu ayenela kutsatila malangizo a m’buku la Gulu Lochita Chifunilo ca Yehova mutu 8, palagilafu 30. Akulu angakambilane ndi mipingo ya m’dziko limene kunacokela abalewo mwa kulemba kalata ndi kuitumiza ku ofesi ya nthambi ya m’dziko lawo kupitila pa jw.org. Poyembekezela, iwo mosamala angafunse abale othaŵa kwawo za mipingo imene anali kusonkhanako, ndi zokhudza utumiki kuti adziŵe umoyo wawo wauzimu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani