LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yesu sanaonetse kuti zimene anthu ananenela mtumikiyu zinali zoona kapena zabodza. Liu la Cigiriki limene linamasulidwa kuti “anamuneneza,” pa Luka 16:1, lingatanthauze kuti mtumikiyu anamunamizila. Koma Yesu anasumika maganizo ake pa zimene mtumikiyu anacita, osati pa mlandu umene anafuna kum’cotsela nchito.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani