LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yosefe amachulidwa kotsiliza m’Malemba pamene Yesu anali na zaka 12. Pamene Yesu anacita cozizwitsa cake coyamba, cimene ndi kusandutsa madzi kukhala vinyo, Yosefe sachulidwako. Iye sachulidwakonso ngakhale pa zocitika zina za pambuyo pake. Panthawi imene Yesu anali pamtengo wozunzikilapo, anapatsa mtumwi Yohane udindo wosamalila Mariya. Yosefe akanakhala kuti anali moyo, Yesu sakanacita zimenezi.—Yoh. 19:26, 27.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani