LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Mkhristu angasankhe kukhala na mfuti n’colinga cakuti aziphela nyama kuti azidya kapena kuti adziteteze ku nyama zolusa. Koma panthawi imene sakuiseŵenzetsa, ayenela kucotsamo mpholopolo, kapenanso kuimasula, ndi kuisungila pa malo otetezeka. Kumene malamulo salola munthu kukhala na mfuti, kapena kumene kuli malamulo a kasewenzetsedwe ka mfuti, Akhristu ayenela kutsatila malamulowo.—Aroma 13:1.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani